Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 13:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 ‘Pakati panu papezeka anthu opanda pake+ amene akufuna kupatutsa anthu mumzinda wawo,+ ponena kuti: “Tiyeni tikatumikire milungu ina,” milungu imene inu simunaidziwe,’

  • 1 Samueli 10:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma anthu opanda pake+ anali kunena kuti: “Kodi ameneyu angatipulumutse bwanji?”+ Chotero anamunyoza,+ moti sanam’bweretsere mphatso iliyonse.+ Koma Sauli anangokhala chete.+

  • 1 Samueli 25:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chonde mbuyanga, musaganizire za Nabala, munthu wopanda pakeyu,+ chifukwa zochita zake ndi zogwirizana ndi dzina lake. Dzina lake ndi Nabala* ndipo ndi wopandadi nzeru.+ Koma ine kapolo wanu wamkazi sindinawaone anyamata amene inu mbuyanga munawatuma.

  • 1 Samueli 30:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma mwamuna aliyense woipa ndi wopanda pake+ mwa amuna onse amene anatsatira Davide anayamba kunena kuti: “Chifukwa chakuti amenewa sanapite nafe, sitiwapatsa zofunkha zimene talanditsazi. Koma aliyense tingomupatsa mkazi wake ndi ana ake basi, awatenge ndipo azipita.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena