Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndipo Samueli anayankha Sauli kuti: “Wamasomphenyayo ndineyo. Tsogola tipite kumalo okwezeka ndipo inuyo mudya ndi ine lero.+ Ndidzakulolani kupita mawa m’mawa, ndipo ndikuuzani zonse zimene mukufuna kudziwa.+

  • 2 Samueli 15:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pamenepo mfumu inapitiriza kuuza Zadoki wansembe kuti: “Iwe ndi wamasomphenya,*+ si choncho kodi? Bwerera kumzinda mu mtendere. Bwerera pamodzi ndi Ahimazi mwana wako wamwamuna ndi Yonatani+ mwana wamwamuna wa Abiyatara. Mubwerere ndi ana anu awiri amene muli nawowa.

  • 1 Mbiri 9:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Onse amene anasankhidwa kuti akhale alonda a pamakomo analipo 212. Iwo anakhala m’midzi yawo+ mogwirizana ndi mndandanda wa mayina wotsatira makolo awo.+ Davide+ ndi Samueli wamasomphenya+ anaika amenewa pa udindo wawo chifukwa cha kukhulupirika kwawo.+

  • 1 Mbiri 29:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Nkhani zokhudza Davide mfumu, zoyambirira ndi zomalizira, zinalembedwa pakati pa mawu a Samueli wamasomphenya,*+ Natani+ mneneri, ndiponso pakati pa mawu a Gadi+ wamasomphenya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena