Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Amuna inu, pitirizani kukonda akazi anu+ monga mmene Khristu anakondera mpingo n’kudzipereka yekha chifukwa cha mpingowo,+

  • 1 Petulo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Inunso amuna,+ pitirizani kukhala ndi akazi anu mowadziwa bwino,+ ndi kuwapatsa ulemu+ monga chiwiya chosalimba, kuti mapemphero anu asatsekerezedwe,+ pakuti mudzalandira nawo limodzi moyo+ umene Mulungu adzakupatseni chifukwa cha kukoma mtima kwake kwakukulu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena