Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Akuitana kumwamba ndi dziko lapansi+

      Kuti apereke chiweruzo kwa anthu ake. Iye akuti:+

  • Salimo 96:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti iye wabwera.+

      Iye wabwera kudzaweruza dziko lapansi.+

      Adzaweruza dziko mwachilungamo,+

      Ndipo adzaweruza mitundu ya anthu mokhulupirika.+

  • Machitidwe 17:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Chifukwa wakhazikitsa tsiku limene akufuna kudzaweruza+ m’chilungamo dziko lapansi kumene kuli anthu, kudzera mwa munthu amene iye wamuika. Ndipo wapereka chitsimikizo kwa anthu onse mwa kumuukitsa+ kwa akufa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena