Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 6:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndipo chiwiya chadothi+ chimene mungawiritsiremo nyamayo muzichiswa. Koma mukawiritsira m’chiwiya chamkuwa, muzichikwecha ndi kuchitsukuluza ndi madzi.

  • Numeri 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Wansembe atenge mwendo wakutsogolo wa nkhosa yamphongo umene wawiritsidwa.+ Atengenso m’dengumo mkate woboola pakati wopanda chofufumitsa, ndi kamkate kopyapyala kopanda chofufumitsa.+ Zinthuzi aziike m’manja mwa Mnaziriyo atameta chizindikiro cha unaziri wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena