Genesis 47:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Ndikufuna ndikagone limodzi ndi makolo anga.+ Choncho udzandinyamule ku Iguputo kuno, ukandiike m’manda a makolo anga.”+ Yosefe anayankha kuti: “Ndidzachitadi monga mwa mawu anu.” Genesis 49:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Atatero anawalamula kuti: “Ine uno ndi ulendo wopita kumene kunapita makolo anga.+ Mukandiike limodzi ndi makolo anga, m’phanga limene lili m’munda wa Efuroni, Mhiti.+ Genesis 50:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Anamunyamula n’kupita naye kudziko la Kanani. Kumeneko anakamuika m’phanga m’munda wa Makipela, woyang’anana ndi munda wa Mamure.+ Mundawo ndi umene Abulahamu anagula kwa Efuroni Mhiti, kuti akhale ndi manda.
30 Ndikufuna ndikagone limodzi ndi makolo anga.+ Choncho udzandinyamule ku Iguputo kuno, ukandiike m’manda a makolo anga.”+ Yosefe anayankha kuti: “Ndidzachitadi monga mwa mawu anu.”
29 Atatero anawalamula kuti: “Ine uno ndi ulendo wopita kumene kunapita makolo anga.+ Mukandiike limodzi ndi makolo anga, m’phanga limene lili m’munda wa Efuroni, Mhiti.+
13 Anamunyamula n’kupita naye kudziko la Kanani. Kumeneko anakamuika m’phanga m’munda wa Makipela, woyang’anana ndi munda wa Mamure.+ Mundawo ndi umene Abulahamu anagula kwa Efuroni Mhiti, kuti akhale ndi manda.