Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano nayi mbiri ya Nowa.

      Nowa anali munthu wolungama.+ Iye anali wopanda cholakwa pakati pa anthu a m’nthawi yake. Nowa anayenda ndi Mulungu woona.+

  • Genesis 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamene Abulamu anali ndi zaka 99, Yehova anaonekera kwa iye n’kumuuza kuti:+ “Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse.+ Yenda pamaso panga ndipo ukhale wolungama.+

  • Deuteronomo 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ukhale wopanda cholakwa pamaso pa Yehova Mulungu wako.+

  • Salimo 84:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa+ ndiponso chishango.+

      Iye amatikomera mtima ndi kutipatsa ulemerero.+

      Yehova samana anthu oyenda mosalakwa chinthu chilichonse chabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena