-
2 Mafumu 10:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Pamenepo Yehu anawalemberanso kalata yachiwiri kuti: “Ngati muli kumbali yanga+ ndipo ngati muzimvera mawu anga, dulani mitu ya ana aamuna+ a mbuye wanu, ndipo mawa nthawi ngati yomwe ino mubwere nayo kwa ine ku Yezereeli.”+
Ana aamuna a mfumuwo, omwe analipo 70, anali ndi akuluakulu a mumzindawo omwe anali kuwasamalira.
-