Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Kenako Davide anatenga mutu+ wa Mfilisiti uja ndi kupita nawo ku Yerusalemu, ndipo zida za Mfilisiti uja anaziika muhema wake.+

  • 1 Samueli 31:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iwo anadula mutu wa Sauli+ ndi kumuvula zida zake. Kenako anatumiza uthenga+ m’dziko lonse la Afilisiti, kunyumba za mafano awo+ ndi kwa anthu awo.

  • 2 Mafumu 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pamenepo Yehu anawalemberanso kalata yachiwiri kuti: “Ngati muli kumbali yanga+ ndipo ngati muzimvera mawu anga, dulani mitu ya ana aamuna+ a mbuye wanu, ndipo mawa nthawi ngati yomwe ino mubwere nayo kwa ine ku Yezereeli.”+

      Ana aamuna a mfumuwo, omwe analipo 70, anali ndi akuluakulu a mumzindawo omwe anali kuwasamalira.

  • Maliko 6:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 n’kuubweretsa m’mbale, ndi kuupereka kwa mtsikana uja. Ndiyeno mtsikanayo anakaupereka kwa mayi ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena