Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anawauza kuti: “Bwererani kumahema anu ndi chuma chambiri ndiponso ziweto zambiri, ndi siliva, golide, mkuwa, zitsulo, ndi zovala zambiri.+ Tengani katundu amene munafunkha+ kwa adani anu n’kugawana ndi abale anu.”

  • 1 Samueli 30:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Choncho Davide anatenga nkhosa zonse ndi ng’ombe zonse za Aamaleki komanso ziweto zonse zimene Aamaleki anawalanda. Kenako iwo anati: “Izi ndi zofunkha za Davide.”+

  • 2 Samueli 3:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Tsopano atumiki a Davide ndi Yowabu, anali kuchokera kunkhondo, atafunkha+ zinthu zambiri. Koma Abineri sanali ndi Davide ku Heburoni popeza anali atanyamuka mwamtendere ndipo anali pa ulendo wake.

  • 2 Samueli 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zinthu zimenezi Mfumu Davide inazipatulira Yehova pamodzi ndi siliva ndi golide wochokera ku mitundu yonse imene inagonjetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena