Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zitatero, m’bale wake Abisalomu+ anamuuza kuti: “Kodi si m’bale wako Aminoni+ amene wakuchitira choipa chimenechi? Tsopano khala chete mlongo wanga. Iyeyo ndi m’bale wako.+ Usadandaule ndi nkhani imeneyi.” Ndiyeno Tamara anayamba kukhala kunyumba ya m’bale wake Abisalomu ndipo sanali kucheza ndi wina aliyense.

  • 2 Samueli 13:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Tsopano mbuyanga mfumu, musavutike mtima ndi mawu amenewa onena kuti, ‘Ana onse a mfumu afa,’ pakuti ndi Aminoni yekha amene wafa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena