Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 42:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Nduna yaikulu ya dzikolo inalankhula nafe mwaukali,+ chifukwa inatiyesa akazitape okafufuza dzikolo.+

  • Miyambo 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuyankha modekha kumabweza mkwiyo,+ koma mawu opweteka amayambitsa mkwiyo.+

  • Miyambo 18:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Munthu wosauka amalankhula mochonderera,+ koma munthu wolemera amayankha mwamphamvu.+

  • Mlaliki 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mawu a m’kamwa mwa munthu wanzeru amakhala osangalatsa,+ koma milomo ya munthu wopusa imamuwononga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena