Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Beni-hadadi+ mfumu ya Siriya anasonkhanitsa gulu lake lonse lankhondo ndiponso mahatchi+ ndi magaleta.+ Atatero ananyamuka pamodzi ndi mafumu ena 32,+ n’kupita kukazungulira+ mzinda wa Samariya+ kuti amenyane nawo.

  • 1 Mafumu 22:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Chotero mfumuyo inafa. Ataibweretsa ku Samariya, anaiika m’manda ku Samariyako.+

  • 2 Mafumu 17:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako mfumu ya Asuri inatenga anthu kuchokera ku Babulo,+ Kuta, Ava,+ Hamati,+ ndi Sefaravaimu+ n’kuwakhazika m’mizinda ya Samariya,+ m’malo mwa ana a Isiraeli. Anthuwo anatenga Samariya n’kumakhala m’mizinda yake.

  • Amosi 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Tsoka kwa anthu amene akukhala mwamtendere+ mu Ziyoni ndiponso anthu amene akumva kuti ndi otetezeka m’phiri la Samariya. Iwo ndiwo anthu olemekezeka a mtundu wotchuka pakati pa mitundu ina, ndipo nyumba yonse ya Isiraeli imabwera kwa anthu amenewa.

  • Machitidwe 8:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma Filipo anapita kumzinda wa Samariya+ ndi kuyamba kulalikira za Khristu kwa anthu akumeneko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena