Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 16:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ahabu mwana wa Omuri anachita zoipa kwambiri pamaso pa Yehova kuposa onse amene anakhalapo iye asanakhale.+

  • 2 Mafumu 8:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iye anayenda m’njira ya anthu a m’nyumba ya Ahabu,+ ndipo anapitiriza kuchita zoipa pamaso pa Yehova+ monga mmene anachitira a m’nyumba ya Ahabu, chifukwa anali wachibale wa nyumba ya Ahabu.+

  • 2 Mbiri 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ahaziya nayenso anayenda m’njira za anthu a m’nyumba ya Ahabu+ chifukwa amayi ake+ ndi amene anali kumulangiza kuti azichita zoipa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena