Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pa nthawiyi, Hezekiya anafunsa Yesaya kuti: “Kodi chizindikiro chakuti Yehova andichiritsa, ndi kuti ndidzapitadi kunyumba ya Yehova pa tsiku lachitatu n’chiyani?”+

  • Salimo 65:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndipo anthu okhala m’madera akutali adzachita mantha ndi zizindikiro zanu,+

      Mudzachititsa kulowa ndi kutuluka kwa dzuwa kufuula mokondwera.+

  • Yesaya 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako.+ Chikhoza kukhala chozama ngati Manda kapena chachitali ngati malo okwera.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena