Genesis 19:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Koma anachititsa khungu amuna amene anali pakhomo la nyumbawo,+ kuyambira wamng’ono kwambiri mpaka wamkulu koposa,+ moti anthuwo anavutika kufufuza khomo.+ Miyambo 4:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Njira ya oipa ili ngati mdima.+ Iwo sadziwa chimene chimawapunthwitsa.+ Yesaya 59:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tikungoyenda ndi khoma ngati anthu akhungu, ndipo tikungofufuzafufuza ngati anthu opanda maso.+ Tapunthwa masanasana ngati kuti tili mu mdima wamadzulo. Pakati pa anthu ojintcha, tikungokhala ngati anthu akufa.+ Yohane 9:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Ndiyeno Yesu ananena kuti: “Ndinabwera m’dziko lino kudzapereka chiweruzo ichi:+ Osaona ayambe kuona,+ ndipo oona akhale akhungu.”+
11 Koma anachititsa khungu amuna amene anali pakhomo la nyumbawo,+ kuyambira wamng’ono kwambiri mpaka wamkulu koposa,+ moti anthuwo anavutika kufufuza khomo.+
10 Tikungoyenda ndi khoma ngati anthu akhungu, ndipo tikungofufuzafufuza ngati anthu opanda maso.+ Tapunthwa masanasana ngati kuti tili mu mdima wamadzulo. Pakati pa anthu ojintcha, tikungokhala ngati anthu akufa.+
39 Ndiyeno Yesu ananena kuti: “Ndinabwera m’dziko lino kudzapereka chiweruzo ichi:+ Osaona ayambe kuona,+ ndipo oona akhale akhungu.”+