1 Mafumu 2:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Kenako Davide anagona limodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide.+ 1 Mafumu 11:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Kenako Solomo anagona pamodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide+ bambo ake. Kenako mwana wake Rehobowamu,+ anayamba kulamulira m’malo mwake. 1 Mafumu 14:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Pomalizira pake, Rehobowamu anagona ndi makolo ake ndipo anaikidwa m’manda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide.+ Mayi ake dzina lawo linali Naama Muamoni.+ Kenako Abiyamu+ mwana wa Rehobowamu anayamba kulamulira m’malo mwake. 2 Mbiri 21:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Patatha zaka ziwiri zathunthu iye akudwala, matumbo ake+ anatuluka ndipo anamwalira ndi matenda oipawa. Anthu ake sanamupserezere zofukiza pa maliro ake ngati mmene anachitira+ pa maliro a makolo ake.
43 Kenako Solomo anagona pamodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide+ bambo ake. Kenako mwana wake Rehobowamu,+ anayamba kulamulira m’malo mwake.
31 Pomalizira pake, Rehobowamu anagona ndi makolo ake ndipo anaikidwa m’manda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide.+ Mayi ake dzina lawo linali Naama Muamoni.+ Kenako Abiyamu+ mwana wa Rehobowamu anayamba kulamulira m’malo mwake.
19 Patatha zaka ziwiri zathunthu iye akudwala, matumbo ake+ anatuluka ndipo anamwalira ndi matenda oipawa. Anthu ake sanamupserezere zofukiza pa maliro ake ngati mmene anachitira+ pa maliro a makolo ake.