Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “‘Ngati mtsogoleri+ wachimwa mwa kuchita mwangozi chimodzi mwa zinthu zimene Yehova Mulungu wake analamula kuti asachite+ ndipo wapalamula,

  • Levitiko 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “‘Munthu akafuna kupereka nsembe yachiyanjano+ kwa Yehova kuti akwaniritse lonjezo lake+ kapena kuti ikhale nsembe yaufulu, azipereka ng’ombe kapena nkhosa yopanda chilema, kuti Mulungu ailandire. Izikhala yopanda chilema chilichonse.

  • 2 Mbiri 7:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako mfumuyo ndi anthu onse anapereka nsembe pamaso pa Yehova.+

  • 2 Mbiri 29:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo anabweretsa ng’ombe zamphongo 7,+ nkhosa zamphongo 7, ana a nkhosa amphongo 7 ndi mbuzi zamphongo 7 kuti azipereke monga nsembe yamachimo+ ya ufumuwo, ya malo opatulika, ndi ya Yuda. Chotero Hezekiya anauza ana a Aroni, omwe anali ansembe,+ kuti apereke nsembeyo paguwa lansembe la Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena