Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova, ine ndimakonda nyumba imene inu mumakhala+

      Ndi malo amene kumakhala ulemerero wanu.+

  • Salimo 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chinthu chimodzi chimene ndapempha kwa Yehova,+

      Chimenecho ndi chimene ndimachikhumba,+

      N’chakuti, ndikhale m’nyumba ya Yehova masiku onse a moyo wanga,+

      Kuti ndione ubwino wa Yehova,+

      Komanso kuti ndiyang’ane kachisi wake moyamikira.+

  • Salimo 122:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 122 Ndinakondwera pamene anandiuza kuti:+

      “Tiyeni tipite+ kunyumba ya Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena