Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mwaipatsa zokhumba za mtima wake,+

      Ndipo simunaimane zokhumba za pakamwa pake.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 66:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndithudi, Mulungu wamva,+

      Wamvetsera mwatcheru mawu a pemphero langa.+

  • Mateyu 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Pemphanibe,+ ndipo adzakupatsani. Pitirizani kufunafuna, ndipo mudzapeza. Gogodanibe,+ ndipo adzakutsegulirani.

  • Mateyu 21:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Chinthu chilichonse chimene mudzapempha m’mapemphero anu, mudzalandira ngati muli ndi chikhulupiriro.”+

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti maso+ a Yehova* ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzero lawo,+ koma nkhope ya Yehova imakwiyira anthu ochita zoipa.”+

  • 1 Yohane 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ifetu timamudalira+ kuti chilichonse chimene tingamupemphe mogwirizana ndi chifuniro chake, amatimvera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena