Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Davide anayamba kukhala m’malo okhala mumpanda wolimba kwambiri, ndipo anawatcha Mzinda wa Davide. Iye anayamba kumanga malo onsewo kuyambira ku Chimulu cha Dothi*+ mpaka mkati.

  • 2 Samueli 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Davide sanafunenso kutenga likasa la Yehova kupita nalo kumene iye anali kukhala, ku Mzinda wa Davide.+ Chotero Davide analipatutsira kunyumba ya Obedi-edomu+ Mgiti.+

  • 1 Mafumu 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Davide anagona limodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena