Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 11:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Zitatero, Davide anatuma nthumwi kukafufuza za mkaziyo.+ Ndiyeno munthu wina ananena kuti: “Kodi ameneyu si Bati-seba+ mwana wa Eliyamu,*+ mkazi wa Uriya+ Mhiti?”+

  • 2 Samueli 11:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamene amuna a mzindawo anatuluka kudzamenyana ndi Yowabu, ena mwa anthu, atumiki a Davide anakanthidwa ndi kugwa, ndipo Uriya Mhiti nayenso anafa.+

  • 2 Samueli 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 N’chifukwa chiyani unanyoza mawu a Yehova mwa kuchita chinthu choipa+ pamaso pake? Uriya Mhiti unamupha ndi lupanga, ndipo mkazi wake unamutenga kukhala mkazi wako,+ pamene Uriyayo unamupha ndi lupanga+ la ana a Amoni.

  • 2 Samueli 23:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 ndi Uriya+ Mhiti, onse pamodzi 37.

  • 1 Mafumu 15:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anatero popeza Davide anachita zoyenera pamaso pa Yehova, ndipo sanapatuke pa chilichonse chimene Mulungu anamulamula masiku onse a moyo wake,+ kupatulapo pa nkhani ya Uriya Mhiti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena