Ezara 4:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Bisilamu, Mitiredati, Tabeeli, ndi anzake ena onse analemba kalata kwa Aritasasita mfumu ya Perisiya m’masiku a mfumuyo. Kalatayo anaimasulira m’Chiaramu n’kuilemba m’zilembo za Chiaramu.+ Ezara 4:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mawu amene analembedwa m’kalata ya mfumu Aritasasita atawerengedwa pamaso pa Rehumu,+ Simusai+ mlembi, ndi anzawo,+ iwo anapita msangamsanga kwa Ayuda ku Yerusalemu n’kukawaletsa ntchitoyo mwankhondo.+ Nehemiya 4:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndiyeno Sanibalati,+ Tobia,+ Aluya,+ Aamoni+ ndi Aasidodi+ atamva kuti ntchito yokonza mpanda wa Yerusalemu ikupita patsogolo, pakuti malo ogumuka anali atayamba kutsekedwa, anakwiya kwambiri. Nehemiya 4:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Komanso adani athu anali kunena kuti: “Sadzadziwa+ kapena kuona kuti tikubwera, kufikira titafika pakati pawo ndipo tidzawapha ndithu ndi kuimitsa ntchito yomangayo.”
7 Bisilamu, Mitiredati, Tabeeli, ndi anzake ena onse analemba kalata kwa Aritasasita mfumu ya Perisiya m’masiku a mfumuyo. Kalatayo anaimasulira m’Chiaramu n’kuilemba m’zilembo za Chiaramu.+
23 Mawu amene analembedwa m’kalata ya mfumu Aritasasita atawerengedwa pamaso pa Rehumu,+ Simusai+ mlembi, ndi anzawo,+ iwo anapita msangamsanga kwa Ayuda ku Yerusalemu n’kukawaletsa ntchitoyo mwankhondo.+
7 Ndiyeno Sanibalati,+ Tobia,+ Aluya,+ Aamoni+ ndi Aasidodi+ atamva kuti ntchito yokonza mpanda wa Yerusalemu ikupita patsogolo, pakuti malo ogumuka anali atayamba kutsekedwa, anakwiya kwambiri.
11 Komanso adani athu anali kunena kuti: “Sadzadziwa+ kapena kuona kuti tikubwera, kufikira titafika pakati pawo ndipo tidzawapha ndithu ndi kuimitsa ntchito yomangayo.”