Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma amuna inu ndinu onamizira anzanu.+

      Nonsenu ndinu madokotala opanda phindu.+

  • Salimo 36:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mawu a pakamwa pake ndi opweteka ndi achinyengo.+

      Wasiya kugwiritsa ntchito nzeru zomuthandiza kuchita zinthu zabwino.+

  • Salimo 38:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthu amene akufuna kundiwononga anditchera misampha,+

      Amene akufuna kundivulaza akulankhula motsutsana nane,+

      Ndipo amakhala akukonza zachinyengo tsiku lonse.+

  • Salimo 52:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Lilime lako limakonza chiwembu, ndipo ndi lakuthwa ngati lezala,+

      Limachita zachinyengo.+

  • Mateyu 12:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ana a njoka inu,+ mungalankhule bwanji zinthu zabwino, pamene muli oipa?+ Pakuti pakamwa pamalankhula zosefukira mumtima.+

  • Yohane 8:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Inu ndinu ochokera kwa atate wanu Mdyerekezi,+ ndipo mukufuna kuchita zokhumba za atate wanu.+ Iyeyo ndi wopha anthu chiyambire kupanduka kwake,+ ndipo sanakhazikike m’choonadi, chifukwa mwa iye mulibe choonadi. Pamene akunena bodza, amalankhula za m’mutu mwake, chifukwa iye ndi wabodza komanso tate wake wa bodza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena