Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Moredekai+ anadziwa zonse zimene zinachitika.+ Choncho anang’amba zovala zake ndi kuvala chiguduli*+ ndipo anadzithira phulusa+ ndi kutuluka kupita pakati pa mzinda. Ndiyeno anayamba kulira mofuula ndiponso mopwetekedwa mtima.+

  • Salimo 65:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Inu Wakumva pemphero, anthu a mitundu yonse adzabwera kwa inu.+

  • Salimo 142:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 142 Ndinafuulira Yehova kuti andithandize.+

      Ndinafuulira Yehova kuti andikomere mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena