Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mbalame zimamanga zisa zawo mmenemo.+

      Dokowe nyumba yake ndiyo mitengo ya mlombwa.+

  • Zekariya 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno ndinakweza maso ndipo ndinaona akazi awiri akubwera. Akaziwo anali kuuluka ndi mapiko ooneka ngati a dokowe ndipo mphepo inali kuwomba mapikowo. Iwo ananyamula chiwiya choyezera chija n’kupita nacho m’mwamba, pakati pa dziko lapansi ndi kumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena