Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Bwenzi atakuuza chinsinsi cha nzeru,

      Chifukwa zinthu za nzeru ndiponso zopindulitsa n’zambiri.

      Komanso bwenzi utadziwa kuti Mulungu wachititsa kuti zolakwa zako zina ziiwalike.+

  • Yobu 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iyetu alibe chikhulupiririro mwa angelo* ake,+

      Ndipo kumwamba si koyera m’maso mwake.+

  • Yobu 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Kodi mwamuna wamphamvu angakhale waphindu kwa Mulungu?+

      Kodi aliyense wozindikira angakhale waphindu kwa iye?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena