Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 62:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndithudi, ana a anthu ochokera kufumbi ali ngati mpweya,+

      Ana a anthu ndi malo othawirako achinyengo.+

      Onse pamodzi akaikidwa pasikelo ndi opepuka kuposa mpweya.+

  • Salimo 144:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Munthu amafanana ndi mpweya wotuluka m’mphuno.+

      Masiku ake ali ngati mthunzi wongodutsa.+

  • Mlaliki 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa chakuti pali zambiri zoyambitsa zinthu zachabe,+ kodi munthu amapindula chiyani?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena