Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndimaganiza kuti: Munthu+ ndani kuti muzimuganizira,+

      Ndipo mwana wa munthu wochokera kufumbi ndani kuti muzimusamalira?+

  • Salimo 103:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Masiku a moyo wa munthu ali ngati masiku a udzu wobiriwira.+

      Iye amaphuka ngati mmene duwa lakutchire limaphukira.+

  • Salimo 144:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, munthu ndani kuti mumuganizire?+

      Kodi mwana wa munthu wochokera kufumbi+ ndani kuti mumuwerengere?

  • Aheberi 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma mboni ina inachitira umboni penapake, kuti: “Munthu ndani kuti muzimuganizira,+ kapena mwana wa munthu ndani kuti muzimusamalira?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena