Salimo 139:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Ndifufuzeni, inu Mulungu, ndi kudziwa mtima wanga.+Ndisanthuleni ndi kudziwa malingaliro anga amene akundisowetsa mtendere,+ Yeremiya 17:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ine Yehova ndimafufuza mtima+ ndi kusanthula impso.+ Munthu aliyense ndimamuchitira zinthu monga mwa zochita zake,+ mogwirizana ndi zipatso za ntchito zake.+
23 Ndifufuzeni, inu Mulungu, ndi kudziwa mtima wanga.+Ndisanthuleni ndi kudziwa malingaliro anga amene akundisowetsa mtendere,+ Yeremiya 17:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ine Yehova ndimafufuza mtima+ ndi kusanthula impso.+ Munthu aliyense ndimamuchitira zinthu monga mwa zochita zake,+ mogwirizana ndi zipatso za ntchito zake.+
10 Ine Yehova ndimafufuza mtima+ ndi kusanthula impso.+ Munthu aliyense ndimamuchitira zinthu monga mwa zochita zake,+ mogwirizana ndi zipatso za ntchito zake.+