Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 18:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mphamvu zake zimachepa,

      Ndipo tsoka+ limakhala likudikira kuti limuyendetse motsimphina.

  • Yesaya 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye adzayang’ana padziko lapansi koma adzangoonapo kuzunzika, mdima,+ kuda, nthawi zovuta ndi zakuda bii, zopanda kuwala.+

  • Yuda 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ali ngatinso mafunde oopsa a panyanja otulutsa thovu la zinthu zoyenera kuwachititsa manyazi,+ ndiponso nyenyezi zosochera, zimene azisungira mdima wandiweyani wosatha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena