Salimo 109:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Kwa iwo ndakhala chinthu choyenera kutonzedwa.+Akandiona amapukusa mitu yawo.+ Mateyu 27:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Tsopano anthu odutsa anayamba kunena mawu onyoza+ Yesu. Anali kupukusa+ mitu yawo