Salimo 83:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Muwathamangitse ndi mphepo yanu yamphamvu,+Ndipo muwasokoneze ndi mphepo yanu yamkuntho.+ Yeremiya 13:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndipo ndidzawombanitsa munthu ndi mnzake, abambo ndi ana awo pa nthawi imodzi,”+ watero Yehova. “Sindidzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni. Ndithu sindidzakhala ndi chifundo choti ndisawawononge.”’+
14 Ndipo ndidzawombanitsa munthu ndi mnzake, abambo ndi ana awo pa nthawi imodzi,”+ watero Yehova. “Sindidzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni. Ndithu sindidzakhala ndi chifundo choti ndisawawononge.”’+