Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Alipo amene sanakonderepo akalonga,

      Ndipo saganizira kwambiri wolemekezeka kuposa wonyozeka,+

      Chifukwa onsewo anapangidwa ndi manja ake.+

  • Salimo 139:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Maso anu anandiona pamene ndinali mluza,+

      Ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu.

      M’bukumo munalembamo za masiku amene zinapangidwa+

      Koma panalibe ngakhale chiwalo chimodzi chimene chinali chitapangidwa.

  • Miyambo 14:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Wobera munthu wosauka mwachinyengo amanyoza amene anamupanga,+ koma wokomera mtima munthu wosauka amalemekeza amene anamupanga.+

  • Miyambo 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Munthu wolemera ndiponso munthu wosauka n’chimodzimodzi.+ Amene anapanga onsewa ndi Yehova.+

  • Malaki 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Kodi tonsefe atate wathu si mmodzi?+ Kodi si Mulungu mmodzi amene anatilenga?+ N’chifukwa chiyani tikuchitirana zachinyengo,+ mwa kuipitsa pangano la makolo athu akale?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena