Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu mwaona mavuto ndi masautso.

      Mumawayang’anabe kuti muchitepo kanthu.+

      Waumphawi,+ mwana wamasiye,* amadziikiza m’manja mwanu.

      Inu mwakhala mthandizi wake.+

  • Salimo 140:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndikudziwa bwino kwambiri kuti Yehova adzazengera+

      Mlandu anthu osautsika. Iye adzachitira chilungamo anthu osauka.+

  • Miyambo 22:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo,+ ndipo adzalanda moyo wa amene akuwabera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena