Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndipo mawu awa amene ndikukulamula lero azikhala pamtima pako,+

  • Salimo 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndimakondwera ndi kuchita chifuniro chanu, inu Mulungu wanga,+

      Ndipo chilamulo chanu chili mumtima mwanga.+

  • Aheberi 8:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “‘Pangano limene ndidzapangana ndi nyumba ya Isiraeli pambuyo pa pangano loyamba lija ndi ili: Ndidzaika malamulo anga m’maganizo mwawo ndi kuwalemba m’mitima yawo.+ Ine ndidzakhala Mulungu wawo+ ndipo iwo adzakhala anthu anga,’+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena