Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi.

      Amabisalira munthu wosalakwa ndi kumupha.+

      ע [ʽAʹyin]

      Maso ake amafunafuna waumphawi.+

  • Luka 19:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Ndipo anali kuphunzitsa m’kachisimo tsiku ndi tsiku. Koma ansembe aakulu, alembi ndi akuluakulu a anthu anafunitsitsa kumupha.+

  • Machitidwe 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Koma chiwembu chawocho chinadziwika kwa Saulo. Komabe iwo anali kuyang’anira mosamala m’zipata zonse usana ndi usiku kuti amuphe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena