Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Lero ndiye mukundipitikitsa pamalo ano ndi pamaso panu.+ Ndidzakhala woyendayenda+ ndi wothawathawa padziko lapansi, ndipo n’zoonekeratu kuti aliyense wondipeza, adzandipha ndithu.”+

  • 2 Mafumu 13:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma Yehova anakomera mtima+ Aisiraeli ndi kuwachitira chifundo+ ndipo anatembenukira kwa iwo chifukwa cha pangano lake+ ndi Abulahamu,+ Isaki,+ ndi Yakobo.+ Iye sanafune kuwawononga+ ndipo sanawachotse pamaso pake mpaka lero.

  • Salimo 102:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa cha kudzudzula kwanu kwamphamvu ndi mkwiyo wanu.+

      Inu mwandikweza m’mwamba kuti munditaye.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena