Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 43:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Ndiweruzeni+ inu Mulungu,

      Weruzani mlandu wanga+ motsutsana ndi mtundu wosakhulupirika.

      Ndipulumutseni kwa munthu wachinyengo ndi wochita zosalungama.+

  • Salimo 99:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye amakonda chilungamo ngati mmene mfumu yamphamvu imachitira.+

      Inu mwakhazikitsa kulungama.+

      Mwakhazikitsa chiweruzo ndi chilungamo pakati pa ana a Yakobo.+

  • Miyambo 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti Wowawombola ndi wamphamvu, ndipo adzawateteza pa mlandu wawo ndi iwe.+

  • Yeremiya 50:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Wowawombola ndi wamphamvu,+ dzina lake ndi Yehova wa makamu.+ Iye sadzalephera kuwaweruzira mlandu wawo+ kuti apumitse dziko lawo+ ndiponso kusokoneza mtendere wa anthu okhala m’Babulo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena