Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Yehova anapanga chilichonse n’cholinga,+ ndipo ngakhale woipa anamusungira tsiku loipa.+

  • Danieli 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamenepo Nebukadinezara anapsera mtima Sadirake, Mesake ndi Abedinego ndipo nkhope yake inasintha. Iye analamula kuti ng’anjoyo aisonkhezere kuwirikiza ka 7 kuposa mmene anali kuchitira nthawi zonse.

  • Danieli 3:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pamenepo Nebukadinezara anati: “Atamandike Mulungu wa Sadirake, Mesake ndi Abedinego+ amene anatumiza mngelo wake+ ndi kupulumutsa atumiki ake amene anamudalira+ ndiponso amene sanamvere mawu a mfumu, koma anali okonzeka kufa chifukwa sanafune kutumikira+ ndi kulambira+ mulungu wina aliyense kupatulapo Mulungu wawo.+

  • Aroma 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komabe, ngati kulungama kwa Mulungu+ kukuonekera chifukwa cha kusalungama kwathu, ndiye tinene kuti chiyani? Kodi tingati Mulungu ndi wosalungama+ poonetsa mkwiyo wake? (Ndikulankhula mmene anthu+ amalankhulira.)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena