Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 34:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mbalame zotchedwa vuwo ndi nungu zidzakhala kumeneko. Komanso akadzidzi a makutu ataliatali ndi akhwangwala azidzakhala kumeneko.+ Iye adzatambasulira dzikolo chingwe choyezera+ malo opanda kanthu, ndiponso miyala yoyezera kuwongoka kwa chinthu.

  • Zefaniya 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Magulu a nyama, nyama zakutchire za m’deralo zidzagona momasuka pakati pa mzindawo.+ Nungu ndiponso mbalame ya vuwo+ zidzagona usiku wonse pakati pa zipilala zakugwa za mzindawo.+ Pawindo padzamveka mawu a nyimbo. Pamakomo a nyumba padzakhala zibuma za nyumba zakugwa, pakuti iye adzakanganula matabwa oyalidwa kukhoma.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena