Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Njenjemerani ndi mantha* pamaso pake, inu anthu nonse okhala padziko lapansi!

      Ndiponso dziko lapansi ndi lokhazikika,

      Silidzagwedezeka ku nthawi zonse.+

  • Yobu 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Amachititsa dziko lapansi kunjenjemera pamalo ake,

      Mwakuti zipilala+ zake zimagwedezeka.

  • Salimo 77:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phokoso la bingu lanu linali ngati la mawilo a galeta.+

      Mphezi zinaunika padziko.+

      Ndipo dziko lapansi linagwedezeka ndi kuyamba kunjenjemera.+

  • Salimo 97:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mphezi zake zinawalitsa dziko lapansi.+

      Dziko linaona ndipo linachita mantha kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena