Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 M’njira zonse za Yehova muli kukoma mtima kosatha ndi choonadi

      Kwa anthu osunga pangano+ lake ndi zikumbutso zake.+

  • Salimo 71:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Inenso ndidzakutamandani ndi chipangizo cha zingwe,+

      Ndidzatamanda choonadi chanu, inu Mulungu.+

      Ndidzaimba nyimbo zokutamandani ndi zeze, Inu Woyera wa Isiraeli.+

  • Salimo 91:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+

      Udzathawira pansi pa mapiko ake.+

      Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.

  • Yesaya 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 M’tsiku limenelo, otsala a Isiraeli+ ndi opulumuka a nyumba ya Yakobo sadzadaliranso yemwe akuwamenya,+ koma ndi mtima wonse adzadalira Yehova, Woyera wa Isiraeli.+

  • Luka 1:55
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 monga momwe anauzira makolo athu akale, Abulahamu ndi mbewu yake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena