Salimo 57:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Moyo wanga uli pakati pa mikango.+Sindingachitire mwina koma kugona pakati pa ana a anthu, amene ali ngati nyama zoopsa zodya anthu,Amene mano awo ali ngati mikondo ndi mivi,+Ndipo lilime lawo lili ngati lupanga lakuthwa.+ Ezekieli 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 “Iwe mwana wa munthu, usawaope.+ Usaope mawu awo ngakhale kuti iwo ndi anthu osamva+ ndipo ali ngati zinthu zokulasa.+ Usaope, ngakhale kuti ukukhala pakati pa zinkhanira.+ Usaope mawu awo+ ndipo usachite mantha ndi nkhope zawo,+ pakuti iwo ndi nyumba yopanduka.+ Mateyu 10:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 “Taonani! Ndikukutumizani monga nkhosa pakati pa mimbulu.+ Chotero khalani ochenjera ngati njoka+ koma oona mtima ngati nkhunda.+
4 Moyo wanga uli pakati pa mikango.+Sindingachitire mwina koma kugona pakati pa ana a anthu, amene ali ngati nyama zoopsa zodya anthu,Amene mano awo ali ngati mikondo ndi mivi,+Ndipo lilime lawo lili ngati lupanga lakuthwa.+
6 “Iwe mwana wa munthu, usawaope.+ Usaope mawu awo ngakhale kuti iwo ndi anthu osamva+ ndipo ali ngati zinthu zokulasa.+ Usaope, ngakhale kuti ukukhala pakati pa zinkhanira.+ Usaope mawu awo+ ndipo usachite mantha ndi nkhope zawo,+ pakuti iwo ndi nyumba yopanduka.+
16 “Taonani! Ndikukutumizani monga nkhosa pakati pa mimbulu.+ Chotero khalani ochenjera ngati njoka+ koma oona mtima ngati nkhunda.+