Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 27:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Yehova, imvani mawu anga pamene ndikuitana.+

      Ndikomereni mtima ndi kundiyankha.+

  • Salimo 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani mawu anga ochonderera pamene ndikufuulira inu kuti mundithandize,

      Pamene ndikukweza manja anga,+ nditayang’ana kumene kuli chipinda chamkati cha m’malo anu opatulika.+

  • Salimo 55:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Inu Mulungu, mvetserani pemphero langa.+

      Musanyalanyaze pempho langa lakuti mundikomere mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena