Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako anauza ana a Isiraeli kuti: “Ana anu akamadzafunsa abambo awo m’tsogolomu kuti, ‘Kodi miyalayi ndi ya chiyani?’+

  • Salimo 71:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ngakhale nditakalamba ndi kumera imvi, inu Mulungu musandisiye,+

      Kufikira nditanena za dzanja lanu lamphamvu ku m’badwo wotsatira,+

      Kufikira nditanena za mphamvu zanu kwa onse obwera m’tsogolo.+

  • Yesaya 38:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Munthu wamoyo, amene akupuma, ndi amene angakutamandeni,+

      Ngati mmene ineyo ndikuchitira lero.+

      Bambo akhoza kuphunzitsa+ ana ake za kukhulupirika kwanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena