Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Inu Yehova Ambuye wathu, dzina lanu ndi lalikulu padziko lonse lapansi,+

      Inuyo ulemerero wanu ukusimbidwa kumwambamwamba!+

  • Salimo 104:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 104 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.+

      Inu Yehova Mulungu wanga, mwasonyeza kuti ndinu wamkulu koposa.+

      Mwadziveka ulemu ndi ulemerero.+

  • Salimo 111:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Zochita zake+ n’zaulemerero ndi ulemu,+

      ו [Waw]

      Ndipo chilungamo chake chidzakhalapobe kwamuyaya.+

  • Salimo 148:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Onse, anthu ndi nyama, atamande dzina la Yehova,+

      Pakuti dzina lake lokhalo lili pamwamba posafikirika.+

      Ulemerero wake uli pamwamba kuposa dziko lapansi ndi kumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena