Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Usapereke umboni wonamizira mnzako.+

  • Salimo 52:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Lilime lako limakonza chiwembu, ndipo ndi lakuthwa ngati lezala,+

      Limachita zachinyengo.+

  • Salimo 57:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Moyo wanga uli pakati pa mikango.+

      Sindingachitire mwina koma kugona pakati pa ana a anthu, amene ali ngati nyama zoopsa zodya anthu,

      Amene mano awo ali ngati mikondo ndi mivi,+

      Ndipo lilime lawo lili ngati lupanga lakuthwa.+

  • Salimo 120:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kodi iwe lilime lachinyengo,+

      Munthu adzakupatsa chiyani ndipo adzawonjezera chiyani pa iwe?

  • Salimo 140:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Anola lilime lawo ndipo lakhala ngati la njoka.+

      M’milomo yawo muli poizoni wa mphiri.+ [Seʹlah.]

  • Yeremiya 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iwo amakunga lilime lawo ngati uta kuti aponye chinyengo,+ koma iwo si okhulupirika m’dzikoli.

      “Iwo anali kuchita zoipa motsatizanatsatizana ndipo anandinyalanyaza,”+ watero Yehova.

  • Yakobo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Lilimenso ndi moto.+ Mwa ziwalo zathu zonse, lilime ndilo lili lodzaza ndi zosalungama chifukwa limadetsa thupi lonse.+ Lili ndi moto wa Gehena* ndipo limayatsa moyo wonse wa munthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena