Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye anamuuza kuti: “Munthu iwe, ndani anandiika ine kukhala woweruza+ kapena wogawa chuma chanu?”

  • 1 Atesalonika 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiponso muyesetse kukhala mwamtendere,+ kusalowerera mu nkhani za eni,+ ndi kugwira ntchito ndi manja anu+ monga mmene tinakulamulirani.

  • 1 Petulo 4:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma pasakhale wina wa inu wovutika+ chifukwa cha kupha munthu, kuba, kuchita choipa china kapena kulowerera nkhani za ena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena