Salimo 27:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Yehova ndiye kuwala+ kwanga ndi chipulumutso changa.+Ndingaopenso ndani?+Yehova ndiye malo a chitetezo cha moyo wanga.+Ndingachitenso mantha ndi ndani?+ Danieli 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Ngati mungatiponyere m’ng’anjo yoyaka moto, Mulungu wathu amene tikumutumikira akhoza kutipulumutsa. Iye atipulumutsa m’ng’anjo yoyaka moto ndiponso m’manja mwanu mfumu.+ Luka 1:74 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 74 kuti pambuyo pakuti tapulumutsidwa m’manja mwa adani,+ atipatse mwayi wochita utumiki wopatulika kwa iye+ mopanda mantha, Yohane 14:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 “Mitima yanu isavutike.+ Khulupirirani Mulungu,+ khulupiriraninso ine.+ Afilipi 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Abale ambiri mwa Ambuye, alimba mtima chifukwa cha kumangidwa kwanga, ndipo akuonetsa kulimba mtima kowonjezereka polankhula mawu a Mulungu mopanda mantha.+
27 Yehova ndiye kuwala+ kwanga ndi chipulumutso changa.+Ndingaopenso ndani?+Yehova ndiye malo a chitetezo cha moyo wanga.+Ndingachitenso mantha ndi ndani?+
17 Ngati mungatiponyere m’ng’anjo yoyaka moto, Mulungu wathu amene tikumutumikira akhoza kutipulumutsa. Iye atipulumutsa m’ng’anjo yoyaka moto ndiponso m’manja mwanu mfumu.+
74 kuti pambuyo pakuti tapulumutsidwa m’manja mwa adani,+ atipatse mwayi wochita utumiki wopatulika kwa iye+ mopanda mantha,
14 Abale ambiri mwa Ambuye, alimba mtima chifukwa cha kumangidwa kwanga, ndipo akuonetsa kulimba mtima kowonjezereka polankhula mawu a Mulungu mopanda mantha.+