Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pambuyo pake Mulungu anafikira Abimeleki usiku m’maloto n’kumuuza kuti: “Ufatu iwe chifukwa cha mkazi amene watengayu,+ pakuti ndi mkazi wa mwini.”+

  • Deuteronomo 22:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Mwamuna akapezeka akugona ndi mkazi wa mwiniwake,+ mwamuna ndi mkaziyo, onsewo azifera pamodzi. Mwamuna wogona ndi mkaziyo ndiponso mkaziyo azifera pamodzi.+ Motero uzichotsa oipawo mu Isiraeli.+

  • 2 Samueli 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pamenepo mkazi wa Uriya anamva kuti Uriya mwamuna wake+ wafa, ndipo anayamba kumulira.+

  • 1 Akorinto 11:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ndiponso mwamuna sanalengedwere mkazi, koma mkazi analengedwera mwamuna.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena